MBIRI YA Malawi

MBIRI YA Malawi Kumvera koma manog'onog'o ayi Timasuke powerenga
tonse ndi amodzi

Tiyambe motere pano #Pa MBIRI YA MALAWI Moni nonse okonda page lino.Tingoti zonse za bwino Mu 2019 muno.NKHAWA Zintha bw...
19/01/2019

Tiyambe motere pano #
Pa MBIRI YA MALAWI

Moni nonse okonda page lino.
Tingoti zonse za bwino
Mu 2019 muno.

NKHAWA
Zintha bwanji apa?
Mfumu chidzowe kuyankhula mozwanyika mtima.
Pakati pa nkhalango ya zizila mudziko la Zambia
Yomwe inali kufupi ndi tsinje wawukulu dzina lake muzizila river.
Ndikuda nkhawa kwambiri mfumu powona kuti tasala wochepa chonchi.
Zowonadi Mr mndowe'
Mfumu chidzowe nayo kusindika pangodya ya Mr mndowe.

DOKO LA SISELI
Poul kanne kulowa mu ofesi ya Mr Gibson luffer.
Zonse zantheka bwana,
Good' Mr kanne
Komano chinthu chimodzi, usayiwale pomwe ukukasinthana ndi Mr Rowland.
Akatenge 250 sojazi, malingana ndi anthu(mamonke) ambiri omwe anthawira ku nkhalango ya zizila sitingakwanitse kuwagwira, chifukwa cha masojazi tili nawo pano Mr kanne.
Chabwino bwana ndava.

ZIZILA FOREST
Mwina tiwoloke tsinjewu kupita tsidya linalo mwina nkhondoyi intha kutipezaso pano ndikutimaliza tonse mfumu chidzowe kuyankhulapo ganizo lake. Chabwino mfumu, nanga poti tsinje uja ndiwawukulu oti ambiri sangakwanise kuwagwira komaso ana Mr mndowe kutsiliramo mfundo yawo.
Eeee!! Mfundo ya bwino Mr mndowe, basi kucha kwa mawa mbandakucha aliyese aziwisidwe kuti tinkhale ndi zokambirana......

Hahaha
MBIRI YA MALAWI
Kubwera ndi m'bebe

Anthu okwana 50 perekani ndemanga zanu kuti MBIRI YA MALAWI ipitirire kapena iyime pazifukwa izi

ZIKOMO nonse.

11/01/2019

Tadzaso makosana
Kodi mwatilandila

Yomwe mukuwerengayi ndi peji ya MZIKA NYASAKUCHOKERA KU BUNGWE LAKAFUKUFUKA LOTCHEDWA  YA MALAWImonthandizidwa ndi websi...
21/04/2017

Yomwe mukuwerengayi ndi peji ya MZIKA NYASA

KUCHOKERA KU BUNGWE LAKAFUKUFUKA LOTCHEDWA
YA MALAWI

monthandizidwa ndi website ya
wwwromzystoryz.com

next page

zinthu zinafika pomvutisisa mu chaka cha 1931 pomwe anthu amasowa pokhala, sikutitu malo kunalibe oti angamangepo mudzi koma chifukwa chankhadza zomwe amati akamangapo mudzi azungu ankhadzawa amabwera kudzagwirapo anthuwa ndikumakawasiya kuchipata cha leki ya Tanzania kuti akadzadzako ndikumawapitisa ku mayiko akuwulaya izitu sizimatengera nyasa yonkha ayi koma afrika yonse,
mphamvu kwa azungu zidali zochuluka kamba koti amadalira mfuti, ukapanga makani sumachedwa kupita nacho chipolopolo, mpaka anthu anasiya kumanga midzi yowoneka chifukwa chamantha ena amagona mumapanga ena amagona munkhalango zowirira kwambiri moti kunalibe kuwopa nyama zolusa koma kungozolowera basi.
Ndipo mavuto ananka akulirakulirabe chifukwa mphamvu kwa munthu okuda zidali zochepa kwambiri zoti nthawi imeneyo angamenye nkhondo ndi azunguwa choncho panalibe kuchitira mwina koma kumankhala mozemba ngati afrika siwawoyi.

Mukuwerengayi ndi MZIKA NYASA

continue....
Chaka cha 1936 kudabuka mkangano wa azungu onkhaonkha kaamba kokuti anthu ambiri amafera pawulendo chifukwa chankhadza zomwe amachitiridwa ndi azungu ena pomawampha mwadala monga kuwaponyera m'madzi, kuwamenya kwambiri ndikusawapasa chakudya mokwanira, moti anthu ambiri amafera njira mudziwa mtunda woyenda ndi sitima yapamadzi kukafika kuwulaya simacheza ayi,
moti kulikulu lawo ena samadziwa zoti anthuwa akumachitiridwa nkhadza zoterezi
moti mkulu woyang'anira za akapolowa bambo Roddin Gavar yemwe anazuzula izi kuti zisinthe azakewomwewo anamukanyanga pankhosi ndikumutengera chuma chake chonse.
Apatu mkuti JOHN CHILEMBWE asanadziwike nkutitu ali wachichepere komatu anali mwana okugwa ndi chisoni pakuwona mtundu m'mene ukunthera, muchaka cha 1939 kunyasalande kunatulukira olemekezeka DR LIVINGSTONE.....

Mukuwerengayi ndi MZIKA NYASA

by YA MALAWI

CONTINUE..

Zikomo awerengi athu potilimbikisa kuti tipitilize kuku pasilani MBIRI YA MALAWI yomwe ikuwuzeni tsatanitsatani waNYASAL...
25/03/2017

Zikomo awerengi athu potilimbikisa kuti tipitilize kuku pasilani MBIRI YA MALAWI yomwe ikuwuzeni tsatanitsatani wa
NYASALANDE.
BUKU LOTSINDIKIZIDWA NDI BUNGWE LAKAFUKUFUKU LOTCHEDWA
lonthandizidwa ndi bungwe la
WWWROMZYSTORYZ.COM

ndi buku lomwe
lalembedwa mwaluso ndi bungwe lakafukufuku lotchedwa
WWWROMZYSTORYZ.COM
ngati mufuna kuwerenga nkhani zopatsa chidwi ndi zosangalasa zambiri fufunzani ku gulu ili
(wwwromzystoryz.com) click here
and read more.....
Osayiwala kupanga like kuti mumve nkhani zambiri.


SEASON 1 (episod 2)
nkhaza komaso nkhondo zinali mbweee! Paliponse kuzungulira africa yonse sikuti inali nyasa yonkha ayi, apatu ngankhale konthawira kunalibe pomwe tamanga mudzi sitimagona koma ku.........like to read more.....

Nkhaniyi ikupitilira ingopangani like ndi comment kuti ipitirire kapena ayi, ngati mwasangalasidwa ndekuti madzulo ano timvere limodzi kuti
atiwuzanji lero kuchokera kuno ku
wwwromzystoryz.com

ndingoti, MWAKOMA NONSE.

31/01/2017

nyimbo zachuluka
oyimba achuluka
akumati akabanda
waku studio
omwa kachasu
nde omvina

mfuso? mkumati
kodi zonsezi
zikufuna zipange
bomba, kapena
zochita zikusowa
amalawife.
tiyankheni amalawi amzanga tidziwe nafe.

ZIKOMO kumpando.

09/04/2016

wwwMBIRyamlw.com

Pa 15 - 04 - 2016 tinkhala tikutsegulira buku la tsopano lomwe mutu wake ndi
yalani mphasa patsikuli kuti tonse tiyambire limodzi, tango layikani kuti tiyambe mwa mkokomo.

  PART 1   Chaka cha 1905 kuno ku nyasa lande kuna li ntendere nthawi imeneyo atsamunda asanabwere timayenda mopanda man...
10/02/2016

PART 1

Chaka cha 1905 kuno ku nyasa lande kuna li ntendere nthawi imeneyo atsamunda asanabwere timayenda mopanda mantha, kunalibe kuwopana. MKuti menemo tikungowopa zilombo zolusa basi, mene tinkafika cha ma 1916 kuno kunyasa lande kunagwa zombe (atsamunda) anthu amenewa anayamba kusowetsa mtendere manyasa omwe ngankhale mfuti samayidziwa ndikomwe mavalidwe amakono,foni,tv,wayilesi ndizina zambiri zogwirisira za chizunguzi. Titafika cha ma 1919 atsamundawa anatenga mphamvu zolamula manyasa onse mwankhanza ndi kusintha dzina la nyasalande kunkhala SOUTHERN RODDISHER Izitu zinachitika kaamba koti panalibe yemwe akanantha kutsutsa powopa kumzuzidwa kapena kumphedwa.... Tiyeni TIWONE KUTSOGOLOKU NYASA ATIUZANJI NGATI MUPAnga ma like okwana 7 or 6 ndi ma comment chimodzimodzi ndidziwa kuti sindili ndenkha ndipitiliza zikomo. okupasirani nkhanizi ndi WWWROMZYSTORYZ.COM

09/01/2016

A m bak nawo

31/10/2015

Kasupe wa Africa yonse ndi dziko liti
(a) lilongwe
(b) zambia
(c) malawi
(d) califonia

26/08/2015

Muli bwanji abale ndi alongo konse komwe muli

ndakulandilani ku bwalo lanu la nkhani zomwe ndiyambe kukupasirani pano pa MBIRI YA MALAWI
pomwe muve nkhani zochuluka

Address

Chirimba Ntc
Kabula

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when MBIRI YA Malawi posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share

Category